Yobu 32:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo amuna atatuwa analeka kumyankha Yobu; pakuti anali wolungama pamaso pake pa iye mwini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo amuna atatuwa analeka kumyankha Yobu; pakuti anali wolungama pamaso pake pa iye mwini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono anthu atatu aja adaleka osamulankhuzanso Yobe, chifukwa choti iyeyo adaadziwona kuti ndi wosachimwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono anthu atatuwa analeka kumuyankha Yobu, chifukwa chakuti iyeyo ankadziona kuti ndi wolungama. Onani mutuwo |