Yobu 3:4 - Buku Lopatulika4 Tsiku lija likhale mdima; Mulungu asalifunse kumwamba, ndi kuunika kusaliwalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tsiku lija likhale mdima; Mulungu asalifunse kumwamba, ndi kuunika kusaliwalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsiku limenelo lisanduke lamdima. Mulungu kumwambako asaliganizirenso tsiku limenelo, kuŵala kusadzaonekenso pa tsikulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsiku limenelo lisanduke mdima; Mulungu wa kumwambako asalilabadirenso; kuwala kusaonekenso pa tsikulo. Onani mutuwo |