Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 3:3 - Buku Lopatulika

3 Litayike tsiku lobadwa ine, ndi usikuwo udati, Waima naye mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Litayike tsiku lobadwa ine, ndi usikuwo udati, Waima naye mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 “Tsiku limene ine ndidabadwa litembereredwe, nawonso usiku umene mai wanga adatenga pathupi pa ine utembereredwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 “Tsiku limene ine ndinabadwa litembereredwe ndi usiku umene ananena kuti, ‘Mwana wamwamuna wabadwa!’

Onani mutuwo Koperani




Yobu 3:3
5 Mawu Ofanana  

Nalankhula Yobu nati,


Tsiku lija likhale mdima; Mulungu asalifunse kumwamba, ndi kuunika kusaliwalire.


Kalanga ine, amai, pakuti mwandibala ine munthu wandeu, munthu wakutetana nalo dziko lonse lapansi! Sindinakongoletsa paphindu, anthu sanandikongoletse paphindu; koma iwo onse anditemberera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa