Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 27:3 - Buku Lopatulika

3 pakuti moyo wanga wonse ukali mwa ine, ndi mpweya wa Mulungu m'mphuno mwanga;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 pakuti moyo wanga wonse ukali mwa ine, ndi mpweya wa Mulungu m'mphuno mwanga;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Nthaŵi zonse pamene ndikupumabe, Mulungu namandipatsa mpweya wa moyo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 nthawi zonse pamene ndili ndi moyo, mpweya wa Mulungu uli mʼmphuno mwanga,

Onani mutuwo Koperani




Yobu 27:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.


M'dzanja mwake muli mpweya wa zamoyo zonse, ndi mzimu wa munthu aliyense.


Koma m'munthu muli mzimu, ndi mpweya wa Wamphamvuyonse wawazindikiritsa.


Mzimu wa Mulungu unandilenga, ndi mpweya wa Wamphamvuyonse umandipatsa moyo.


Siyani munthu, amene mpweya wake uli m'mphuno mwake; chifukwa m'mene awerengedwamo ndi muti?


satumikiridwa ndi manja a anthu, monga wosowa kanthu, popeza Iye mwini apatsa zonse moyo ndi mpweya ndi zinthu zonse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa