Yobu 26:4 - Buku Lopatulika4 Wafotokozera yani mau? Ndi mzimu wa yani unatuluka mwa iwe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Wafotokozera yani mau? Ndi mzimu wa yani unatuluka mwa iwe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kodi ndani adzamva mau akoŵa? Nanga udazitenga kuti zonsezi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako? Onani mutuwo |