Yobu 26:3 - Buku Lopatulika3 Wampangira bwanji wopanda nzeruyu! Ndi kudziwitsa nzeru zenizeni mochuluka! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Wampangira bwanji wopanda nzeruyu! Ndi kudziwitsa nzeru zenizeni mochuluka! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi wandilangiza zabwino ine, munthu wopanda nzerune ngati? Kodi wandiwuza nzeru zambiri pamenepa ngati? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka! Onani mutuwo |