Yobu 26:2 - Buku Lopatulika2 Wamthandiza bwanji wopanda mphamvu. Kulipulumutsa dzanja losalimba! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Wamthandiza bwanji wopanda mphamvu. Kulipulumutsa dzanja losalimba! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Iwe, kodi wandithandiza ine munthu wosauka ndi wofookane ngati? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka! Onani mutuwo |