Yobu 22:8 - Buku Lopatulika8 Koma munthu mwini mphamvu, dziko ndi lake; ndi munthu wovomerezeka, anakhala momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma munthu mwini mphamvu, dziko ndi lake; ndi munthu wovomerezeka, anakhala momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chifukwa cha mphamvu zako udalanda dziko lalikulu, chifukwa cha kudzikonda udakhazikika m'menemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 ngakhale unali munthu wamphamvu, wokhala ndi malo akeake, munthu waulemu wake, wokhala mʼdzikomo. Onani mutuwo |