Yobu 22:3 - Buku Lopatulika3 Kodi Wamphamvuyonse akondwera nako kuti iwe ndiwe wolungama? Kapena kodi apindula nako kuti ukwaniritsa njira zako? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kodi Wamphamvuyonse akondwera nako kuti iwe ndiwe wolungama? Kapena kodi apindula nako kuti ukwaniritsa njira zako? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi Mphambe angapeze bwino chifukwa cha kulungama kwako? Kodi kapena Iyeyo nkupindulapo kanthu pa makhalidwe ako angwirowo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kodi Wamphamvuzonse akanapeza chabwino chotani iweyo ukanakhala wolungama? Kodi iyeyo akanapeza phindu lanji makhalidwe ako akanakhala angwiro? Onani mutuwo |