Yobu 22:10 - Buku Lopatulika10 Chifukwa chake misampha ikuzinga. Ndi mantha akuvuta modzidzimutsa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chifukwa chake misampha ikuzinga. Ndi mantha akuvuta modzidzimutsa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nchifukwa chake misamphayi yakuzinga, ndipo wadzidzimuka ndi mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Nʼchifukwa chake misampha yakuzungulira, nʼchifukwa chake tsoka ladzidzidzi lakuchititsa mantha, Onani mutuwo |