Yobu 20:3 - Buku Lopatulika3 Ndamva kudzudzula kwakundichititsa manyazi, ndi mzimu wa nzeru yanga undiyankha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndamva kudzudzula kwakundichititsa manyazi, ndi mzimu wa nzeru yanga undiyankha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndikumva mau ondidzudzula ndi ondinyoza, koma ndadziŵa kale m'mene ndingathe kuyankhira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndikumva kudzudzula kondinyoza, ndipo kumvetsetsa kwanga kwa zinthu kwandifulumiza kuti ndiyankhe. Onani mutuwo |