Yobu 20:2 - Buku Lopatulika2 M'mwemo zolingirira zanga zindiyankha, chifukwa chake ndifulumidwa m'kati mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 M'mwemo zolingirira zanga zindiyankha, chifukwa chake ndifulumidwa m'kati mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Iwe Yobe, wandipsetsa mtima. Nchifukwa chake ndikufulumira kuyankha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Kuvutika kwa mʼmaganizo kwanga kwandifulumiza kuti ndiyankhe chifukwa ndasautsidwa kwambiri. Onani mutuwo |