Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 20:2 - Buku Lopatulika

2 M'mwemo zolingirira zanga zindiyankha, chifukwa chake ndifulumidwa m'kati mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 M'mwemo zolingirira zanga zindiyankha, chifukwa chake ndifulumidwa m'kati mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Iwe Yobe, wandipsetsa mtima. Nchifukwa chake ndikufulumira kuyankha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Kuvutika kwa mʼmaganizo kwanga kwandifulumiza kuti ndiyankhe chifukwa ndasautsidwa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 20:2
15 Mawu Ofanana  

Ndaniyo adzatsutsana nane? Ndikakhala chete, ndidzapereka mzimu wanga.


Pamenepo anayankha Zofari Mnaama, nati,


Ndamva kudzudzula kwakundichititsa manyazi, ndi mzimu wa nzeru yanga undiyankha.


Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao chisoni? Koma akhoza ndani kudziletsa kunena?


Pofulumizidwa mtima ndinati ine, anthu onse nga mabodza.


Ndipo ine, pakutenga nkhawa, ndinati, Ndadulidwa kundichotsa pamaso panu. Komatu munamva mau a kupemba kwanga pamene ndinafuulira kwa Inu.


Wosakwiya msanga apambana kumvetsa; koma wansontho akuza utsiru.


Kodi uona munthu wansontho m'mau ake? Ngakhale chitsiru chidzachenjera, koma ameneyo ai.


Usakangaze mumtima mwako kukwiya; pakuti mkwiyo ugona m'chifuwa cha zitsiru.


Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso.


Ndipo pomwepo analowa m'mangum'mangu kwa mfumu, napempha kuti, Ndifuna kuti mundipatse tsopano apa, mutu wake wa Yohane Mbatizi mumbale.


Pakuti ndiwachitira iwo umboni kuti ali ndi changu cha kwa Mulungu, koma si monga mwa chidziwitso.


Mudziwa, abale anga okondedwa, kuti munthu aliyense akhale wotchera khutu, wodekha polankhula, wodekha pakupsa mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa