Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 20:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo anayankha Zofari Mnaama, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo anayankha Zofari Mnaama, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Zofari wa ku Naama adayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti

Onani mutuwo Koperani




Yobu 20:1
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo anayankha Zofari wa ku Naama, nati,


muchite nalo mantha lupanga; pakuti mkwiyo utenga zolakwa za lupanga, kuti mudziwe pali chiweruzo.


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


M'mwemo zolingirira zanga zindiyankha, chifukwa chake ndifulumidwa m'kati mwanga.


Namuka Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, nachita monga Yehova adawauza; ndipo Yehova anavomereza Yobu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa