Yobu 2:9 - Buku Lopatulika9 Pamenepo mkazi wake ananena naye, Kodi uumiriranso kukhala wangwiro? Chitira Mulungu mwano, ufe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pamenepo mkazi wake ananena naye, Kodi uumiriranso kukhala wangwiro? Chitira Mulungu mwano, ufe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono mkazi wake adamuuza kuti, “Ha! Mukukhalabe okhulupirika motere! Ingomtukwanani Mulunguyo, mufe basi!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mkazi wake anati kwa iye, “Kodi ukuwumirirabe kukhala wangwiro? Tukwana Mulungu kuti ufe!” Onani mutuwo |