Yobu 2:7 - Buku Lopatulika7 Natuluka Satana pamaso pa Yehova, nazunza Yobu ndi zilonda zowawa, kuyambira kuphazi lake kufikira pakati pamutu pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Natuluka Satana pamaso pa Yehova, nazunza Yobu ndi zilonda zowawa, kuyambira kuphazi lake kufikira pakati pamutu pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Choncho Satana adachoka kumsiya Chauta napita kukazunza Yobe ndi zilonda zoopsa pa thupi lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho Satana anachoka pamaso pa Yehova napita kukazunza Yobu ndi zilonda zaululu pa thupi lake lonse. Onani mutuwo |