Yobu 2:4 - Buku Lopatulika4 Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Khungu kulipa khungu, inde munthu adzapereka zonse ali nazo kuombola moyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Khungu kulipa khungu, inde munthu adzapereka zonse ali nazo kuombola moyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Apo Satana adayankha kuti, “Koma ayesedwe m'thupi mwake. Zinthu zonse zimene munthu ali nazo angathe kuzipereka, chikulu iyeyo ali moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Satana anayankha kuti, “Iye ayesedwe mʼthupi mwake. Munthu angathe kupereka zonse ali nazo malingana iyeyo ali ndi moyo. Onani mutuwo |