Yobu 19:9 - Buku Lopatulika9 Anandivula ulemerero wanga, nandichotsera korona pamutu panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anandivula ulemerero wanga, nandichotsera korona pamutu panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Iye wandilanda ulemerero wanga, wandivula chisoti chaulemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye wandilanda ulemu wanga ndipo wandivula chipewa chaufumu pamutu panga. Onani mutuwo |