Yobu 18:3 - Buku Lopatulika3 Tiyesedwa bwanji ngati nyama zakuthengo, ndi kukhala odetsedwa pamaso panu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Tiyesedwa bwanji ngati nyama za kuthengo, ndi kukhala odetsedwa pamaso panu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chifukwa chiyani ukutiyesa opusa ngati ng'ombe? Chifukwa chiyani tikuwoneka ngati opanda nzeru m'maso mwako? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Chifukwa chiyani ukutiyesa ngati ngʼombe ndi kuoneka ngati opusa mʼmaso mwako? Onani mutuwo |