Yobu 17:5 - Buku Lopatulika5 Iye wakupereka mabwenzi ake ku ukapolo, m'maso mwa ana ake mudzada. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Iye wakupereka mabwenzi ake ku ukapolo, m'maso mwa ana ake mudzada. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Paja akuti munthu akapereka abwenzi ake chifukwa cha chuma, ana ake amazunzika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi. Onani mutuwo |