Yobu 17:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti mwabisira mtima wao nzeru; chifukwa chake simudzawakuza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti mwabisira mtima wao nzeru; chifukwa chake simudzawakuza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Inu mwatseka mitima yao kuti asamvetsetse bwino zanzeru, choncho musalole kuti iwowo apambane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane. Onani mutuwo |