Yobu 16:7 - Buku Lopatulika7 Koma tsopano wandilemetsa Iye; mwapasula msonkhano wanga wonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma tsopano wandilemetsa Iye; mwapasula msonkhano wanga wonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndithudi, Mulungu wanditha mphamvu, waononga banja langa lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndithudi, Inu Mulungu mwanditha mphamvu; mwawononga banja langa lonse. Onani mutuwo |