Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 16:6 - Buku Lopatulika

6 Chinkana ndinena chisoni changa sichitsika; ndipo ndikaleka, chindichokera nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Chinkana ndinena chisoni changa sichitsika; ndipo ndikaleka, chindichokera nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 “Ine ndikati ndilankhule, zoŵaŵa zanga sizichepa. Ndikati ndikhale chete, zoŵaŵazo zikhala zilipobe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 “Koma ine ndikati ndiyankhule ululu wanga sukuchepa; ndipo ndikati ndikhale chete, ululu wanga sukuchokabe.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 16:6
6 Mawu Ofanana  

Mtima wanga ulema nao moyo wanga, ndidzadzilolera kudandaula kwanga, ndidzalankhula pakuwawa mtima wanga.


Koma ndikadakulimbikitsani ndi m'kamwa mwanga, ndi chitonthozo cha milomo yanga chikadatsitsa chisoni chanu.


Ndikati, Ndidzaiwala chondidandaulitsa, ndidzasintha nkhope yanga yachisoni, ndidzasekerera.


Pamenepo ndiopa zisoni zanga zonse, ndidziwa kuti simudzandiyesa wosachimwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa