Yobu 16:3 - Buku Lopatulika3 Kodi adzatha mau ouluzika? Kapena chikuwindula nchiyani kuti uyankha zotere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kodi adzatha mau ouluzika? Kapena chikuwindula nchiyani kuti uyankha zotere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi mudzakhala mukulankhulabe mau achabechabeŵa mpaka liti? Kaya chakuvutani nchiyani kuti muzilankhulabe mau otsutsaŵa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kodi mawu anu ochulukawo adzatha? Kodi chikukuvutani nʼchiyani kuti muzingoyankhula mawu otsutsawa? Onani mutuwo |