Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 15:9 - Buku Lopatulika

9 Udziwa chiyani, osachidziwa ife? Uzindikira chiyani, chosakhala mwa ife?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Udziwa chiyani, osachidziwa ife? Uzindikira chiyani, chosakhala mwa ife?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kodi nchiyani chimene umadziŵa iwe, chosachidziŵa ife? Kodi chilipo chimene umamvetsa iwe, chosachimvetsa ife?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kodi iwe umadziwa chiyani chimene ife sitichidziwa? Kodi iwe uli ndi chidziwitso chanji chimene ife tilibe?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 15:9
7 Mawu Ofanana  

Koma inenso ndili nayo nzeru monga inu. Sindingakuchepereni; ndani sadziwa zonga izi?


Chimene muchidziwa inu, inenso ndichidziwa; sindikucheperani.


Pakuti ndani waima mu upo wa Yehova, kuti aone namve mau ake? Ndani wazindikira mau anga, nawamva?


Kodi mupenyera zopenyeka pamaso? Ngati wina alimbika mwa yekha kuti ali wa Khristu, ayesere ichinso mwa iye yekha, kuti monga iye ali wa Khristu, koteronso ife.


Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewere konse ndi atumwi oposatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa