Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 15:1 - Buku Lopatulika

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Apo Elifazi wa ku Temani adayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yobu 15:1
7 Mawu Ofanana  

Koma thupi lake limuwawira yekha, ndi mtima wake umliritsa yekha.


Kodi mwini nzeru ayankhe ndi kudziwa kouluzika, ndi kudzaza mimba yake ndi mphepo ya kum'mawa?


Atamva tsono mabwenzi atatu a Yobu za choipa ichi chonse chidamgwera, anadza, yense kuchokera kwao, Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, napangana kudzafika kumlirira ndi kumsangalatsa.


Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,


Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati,


Kunali tsono atanena Yehova mau awa kwa Yobu, Yehova anati kwa Elifazi wa ku Temani, Mkwiyo wanga wakuyakira iwe ndi mabwenzi ako awiri, pakuti simunandinenere choyenera monga ananena mtumiki wanga Yobu.


Namuka Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofari wa ku Naama, nachita monga Yehova adawauza; ndipo Yehova anavomereza Yobu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa