Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 13:8 - Buku Lopatulika

8 Kodi mukhalira kumodzi ndi Iye? Kodi mungamuimilire Mulungu pa mlandu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Kodi mukhalira kumodzi ndi Iye? Mundilimbirana mwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kodi mukuti mukondere Mulungu? Kodi mukuti muteteze Mulungu pa mlandu wake?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Kodi mudzaonetsa kuti Iyeyo ngokondera? Kodi inu mudzamuteteza Mulungu pa mlandu wake?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 13:8
7 Mawu Ofanana  

Adzakudzudzulani ndithu, mukachita tsankho m'tseri.


Ndisati ndisamalire nkhope ya munthu, kapena kumtchula munthu maina omdyola nao;


Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo ntchito ya manja ake.


Izinso zili za anzeru, poweruza chetera silili labwino.


Musamachita chisalungamo pakuweruza mlandu; usamavomereza munthu wosauka, kapena kulemekeza munthu womveka; uweruze mlandu wa munthu mnzako molungama.


Chifukwa chake Inenso ndakuikani onyozeka ndi ochepseka kwa anthu onse, popeza simunasunge njira zanga, koma munaweruza mwankhope pochita chilamulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa