Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 13:6 - Buku Lopatulika

6 Tamvani tsono kudzikanira kwanga, tamverani kudzinenera kwa milomo yanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Tamvani tsono kudzikanira kwanga, tamverani kudzinenera kwa milomo yanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono mumve zimene nditi ndinene, mumvere mau anga ofotokoza za mlandu wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Tsopano imvani kudzikanira kwanga; imvani kudandaula kwa pakamwa panga.

Onani mutuwo Koperani




Yobu 13:6
8 Mawu Ofanana  

Mvetsetsani mau anga, ndi kunenetsa kwanga kumveke m'makutu mwanu.


Mwenzi mutakhala chete konse, ndiko kukadakhala nzeru zanu.


Kodi munenera Mulungu mosalungama, ndi kumnenera Iye monyenga?


Tamverani mau anga, inu anzeru; munditcherere khutu inu akudziwa.


Ndipo atamuuza Yotamu, anamuka iye naimirira pamutu paphiri la Gerizimu, nakweza mau ake, nafuula, nanena nao, Mundimvere ine, eni ake a ku Sekemu inu, kuti Mulungu amvere inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa