Yobu 13:2 - Buku Lopatulika2 Chimene muchidziwa inu, inenso ndichidziwa; sindikucheperani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chimene muchidziwa inu, inenso ndichidziwa; sindikucheperani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Zimene inu mumadziŵa, inenso ndimazidziŵa. Inu simundipambana ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Zimene inu mukudziwa, inenso ndimazidziwa; ineyo sindine munthu wamba kwa inu. Onani mutuwo |