Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yobu 12:3 - Buku Lopatulika

3 Koma inenso ndili nayo nzeru monga inu. Sindingakuchepereni; ndani sadziwa zonga izi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Koma inenso ndili nayo nzeru monga inu. Sindingakuchepereni; ndani sadziwa zonga izi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu nomwe. Inu simundipambana, ai. Aliyense amadziŵa zonse mwanenazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu; ineyo sindine munthu wamba kwa inu. Ndani amene sadziwa zonse zimene mwanenazi?

Onani mutuwo Koperani




Yobu 12:3
7 Mawu Ofanana  

Udziwa chiyani, osachidziwa ife? Uzindikira chiyani, chosakhala mwa ife?


Usayankhe chitsiru monga mwa utsiru wake, kuti ungafanane nacho iwe wekha.


Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewere konse ndi atumwi oposatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa