Yobu 11:5 - Buku Lopatulika5 Koma, ha? Mwenzi atanena Mulungu, ndi kukutsegulira milomo yake motsutsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma, ha? Mwenzi atanena Mulungu, ndi kukutsegulira milomo yake motsutsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma ha, achikhala Mulungu adaalankhula, achikhala adaakudzudzula, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aa, nʼkanakonda Mulungu akanayankhula kuti Iye atsekule pakamwa pake kutsutsana nawe Onani mutuwo |