Yobu 11:2 - Buku Lopatulika2 Kodi mau ochulukawa sayenera kuwayankha? Ndi munthu wa milomo ayenera kuyesedwa wolungama? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Kodi mau ochulukawa sayenera kuwayankha? Ndi munthu wa milomo ayenera kuyesedwa wolungama? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Kodi mau ambirimbiriŵa nkukhala osaŵayankha? Kodi kulongolola nkumulungamitsa munthu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Kodi mawu ambirimbiriwa nʼkukhala osayankhidwa? Kodi munthu woyankhulayankhulayu nʼkulungamitsidwa? Onani mutuwo |