Yobu 10:8 - Buku Lopatulika8 Manja anu anandiumba, nandiulunga monsemu, koma mufuna kundiononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Manja anu anandiumba, nandiulunga monsemu, koma mufuna kundiononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Mudandiwumba ndi kundipanga ndi manja anu. Koma tsopano mukufuna kundiwononga ndi manja anu omwewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Munandiwumba ndi kundipanga ndi manja anu. Kodi tsopano Inu mudzatembenuka ndi kundiwononga? Onani mutuwo |