Yobu 10:3 - Buku Lopatulika3 Chikukomerani kodi kungosautsa, kuti mupeputsa ntchito yolemetsa manja anu, ndi kuti muwalira pa uphungu wa oipa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chikukomerani kodi kungosautsa, kuti mupeputsa ntchito yolemetsa manja anu, ndi kuti muwalira pa uphungu wa oipa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi inu zikukukomerani kuti mundizunze ndi kundinyoza ine, ntchito ya manja anune, chonsecho mukukondera upo wa anthu oipa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kodi mumakondwera mukamandizunza, kunyoza ntchito ya manja anu, chonsecho mukusekerera ndi zochita za anthu oyipa? Onani mutuwo |