Yobu 10:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzati kwa Mulungu, Musanditsutse; mundidziwitse chifukwa cha kutsutsana nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzati kwa Mulungu, Musanditsutse; mundidziwitse chifukwa cha kutsutsana nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzauza Mulungu kuti, Inu Mulungu, musandiweruze kuti ndine wolakwa. Koma mundidziŵitse chifukwa chimene mukukanganirana nane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzati kwa Mulungu wanga: Musandiweruze kuti ndine wolakwa, koma mundiwuze chifukwa chimene Inu mukukanganira ndi ine. Onani mutuwo |