Yobu 1:9 - Buku Lopatulika9 Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Kodi Yobu aopa Mulungu pachabe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Kodi Yobu aopa Mulungu pachabe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Satana adafunsa Chauta kuti, “Kani mwayesa Yobe uja amangokumverani pachabe? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Satana anayankha kuti, “Kodi Yobu amaopa Mulungu popanda chifukwa?” Onani mutuwo |