Yesaya 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndidzadzitengera ine mboni zokhulupirika, Uriya wansembe, ndi Zekariya mwana wa Yeberekiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndidzadzitengera ine mboni zokhulupirika, Uriya wansembe, ndi Zekariya mwana wa Yeberekiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono ndidapeza mboni zokhulupirika, wansembe Uriya ndiponso Zekariya mwana wa Yeberekiya, kuti andichitire umboni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ndidzayitana wansembe Uriya ndi Zekariya mwana wa Yeberekiya kuti akhale mboni zanga zodalirika.” Onani mutuwo |