Yeremiya 9:25 - Buku Lopatulika25 Taonani, masiku alikudza, ati Yehova, kuti ndidzalanga onse odulidwa m'kusadulidwa kwao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Taonani, masiku alikudza, ati Yehova, kuti ndidzalanga onse odulidwa m'kusadulidwa kwao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Chauta akunena kuti, “Nthaŵi ikubwera pamene ndidzalanga onse oumbalidwa, amene mu mtima sasamalako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 “Nthawi ikubwera,” akutero Yehova, “pamene ndidzalanga onse amene anachita mdulidwe koma mu mtima sasamala nʼkomwe. Onani mutuwo |