Yeremiya 9:22 - Buku Lopatulika22 Nenani, atero Yehova, Mitembo yathu idzagwa ngati ndowe pamunda, ndi monga chipukutu pambuyo pa wakusenga, palibe wochitola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Nenani, atero Yehova, Mitembo yathu idzagwa ngati ndowe pamunda, ndi monga chipukutu pambuyo pa wakusenga, palibe wochitola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Chauta adandiwuza kuti ndinene izi: “Mitembo ya anthu idzagwa, kuchita kuti mbwembwembwe ngati ndoŵe m'minda, ngati mitolo pambuyo pa anthu ovuna. Koma palibe amene adzaitole.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Yehova anandiwuza kuti ndinene izi kuti, “ ‘Mitembo ya anthu idzakhala ili lambalamba ngati ndowe mʼminda, ngati mapesi mʼmbuyo mwa wokolola, popanda munthu woyitola.’ ” Onani mutuwo |