Yeremiya 9:20 - Buku Lopatulika20 Koma imvani mau a Yehova, akazi inu, khutu lanu lilandire mau a pakamwa pake, phunzitsani ana anu akazi kulira, ndi yense aphunzitse mnzake maliridwe ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma imvani mau a Yehova, akazi inu, khutu lanu lilandire mau a pakamwa pake, phunzitsani ana anu akazi kulira, ndi yense aphunzitse mnzake maliridwe ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ine ndidati, “Inu azimai, mverani mau a Chauta. Tcherani makutu kuti mumve zimene akunena. Ana anu aakazi muŵaphunzitse kulira. Aliyense aphunzitse mnzake nyimbo yamaliro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsono inu amayi, imvani mawu a Yehova; tcherani makutu anu kuti mumve mawu a Yehova. Phunzitsani ana anu aakazi kulira mwachisoni; aliyense aphunzitse mnzake nyimbo ya maliro. Onani mutuwo |