Yeremiya 9:19 - Buku Lopatulika19 Pakuti mau a kulira amveka mu Ziyoni, Tafunkhidwa, tanyazitsidwa, pakuti tasiya dziko, pakuti agwetsa zokhalamo zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pakuti mau a kulira amveka m'Ziyoni, Tafunkhidwa, tanyazitsidwa, pakuti tasiya dziko, pakuti agwetsa zokhalamo zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Kukumveka kulira kwa Ziyoni, akuti, “Kalanga ife! Taonongeka! Manyazi aakulu atigwera. Tiyenera kusiya dziko lathu, chifukwa nyumba zathu azigwetsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kulira mwachisoni kukumveka kuchokera mu Ziyoni akuti, ‘Aa! Ife tawonongeka! Tachita manyazi kwambiri! Tiyenera kuchoka mʼdziko lathu chifukwa atipirikitsa mʼnyumba zathu.’ ” Onani mutuwo |