Yeremiya 9:18 - Buku Lopatulika18 afulumire, atikwezere ife mau a maliro, kuti maso athu agwe misozi, ndi zikope zathu ziyendetse madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 afulumire, atikwezere ife mau a maliro, kuti maso athu agwe misozi, ndi zikope zathu ziyendetse madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Anthu akuti, “Abwere mofulumira adzatilire kuti m'maso mwathu mudze misozi nsidze zathu zinyowe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Anthu akuti, “Abwere mofulumira kuti adzatilire mpaka mʼmaso mwathu mutatuluka misozi ndi kuti msidze zathu zinyowe ndi madzi. Onani mutuwo |