Yeremiya 9:17 - Buku Lopatulika17 Atero Yehova wa makamu, Kumbukirani inu, ndi kuitana akazi akulira, adze; aitaneni akazi ochenjera, kuti adze; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Atero Yehova wa makamu, Kumbukirani inu, ndi kuitana akazi akulira, adze; aitaneni akazi ochenjera, kuti adze; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chauta Wamphamvuzonse akunena kuti, “Muziganize bwino, muitane akazi olira maliro kuti abwere. Akaziwo akhale aja amadziŵa kwambiri kuliraŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Tsopano ganizirani! Muyitane akazi olira mwachisoni kuti abwere; itanani akazi odziwa kulira bwino.” Onani mutuwo |