Yeremiya 9:16 - Buku Lopatulika16 Ndidzawabalalitsanso mwa amitundu, amene iwo kapena makolo ao sanawadziwe; ndipo ndidzatumiza lupanga, liwatsate mpaka ndawatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndidzawabalalitsanso mwa amitundu, amene iwo kapena makolo ao sanawadziwa; ndipo ndidzatumiza lupanga, liwatsate mpaka ndawatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndidzaŵabalalitsa pakati pa mitundu ya anthu imene iwowo kapena makolo ao sadaidziŵe. Ndidzaŵalondola ndi ankhondo mpaka kuŵatheratu onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndidzawabalalitsa pakati pa mitundu ya anthu imene iwowo kapena makolo awo sanayidziwe, ndipo ndidzawalondola ndi ankhondo mpaka nditawawononga.” Onani mutuwo |