Yeremiya 9:14 - Buku Lopatulika14 koma anatsata kuuma kwa mtima wao, ndi Baala, monga makolo ao anawaphunzitsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma anatsata kuuma kwa mtima wao, ndi Baala, monga makolo ao anawaphunzitsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma ankangotsata zolakwa za mitima yao yokanika. Ankapembedza Abaala monga momwe makolo ao adaŵaphunzitsira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mʼmalo mwake, anatsatira zolakwa za mʼmitima yawo; anapembedza Abaala ngati momwe makolo awo anawaphunzitsira.” Onani mutuwo |
Koma tidzachita ndithu mau onse anatuluka m'kamwa mwathu, kufukizira mfumu yaikazi ya kumwamba, ndi kumthirira iye nsembe zothira, monga momwe tinkachitira ife, ndi atate athu, ndi mafumu athu ndi akulu athu, m'mizinda ya Yuda, ndi m'miseu ya Yerusalemu, pakuti pamenepo tinali ndi chakudya chokwanira, tinakhala bwino, sitinaona choipa.