Yeremiya 8:22 - Buku Lopatulika22 Kodi mulibe vunguti mu Giliyadi? Kodi mulibe sing'anga m'menemo; analekeranji kuchira mwana wamkazi wa anthu anga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Kodi mulibe vunguti m'Giliyadi? Kodi mulibe sing'anga m'menemo; analekeranji kuchira mwana wamkazi wa anthu anga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kodi ku Giliyadi kulibe mankhwala ochiritsa? Kodi kumeneko kulibe sing'anga? Chifukwa chiyani mabala a anthu anga sadapole? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kodi ku Giliyadi kulibe mankhwala ochiritsa? Kodi kumeneko kulibe singʼanga? Nanga chifukwa chiyani mabala a anthu anga sanapole? Onani mutuwo |