Yeremiya 8:20 - Buku Lopatulika20 Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Anthu akuti, “Kholola lapita, chilimwe chapita, koma sitidapulumukebe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Nthawi yokolola yapita, chilimwe chapita, koma sitinapulumuke.” Onani mutuwo |