Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 8:20 - Buku Lopatulika

20 Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Anthu akuti, “Kholola lapita, chilimwe chapita, koma sitidapulumukebe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 “Nthawi yokolola yapita, chilimwe chapita, koma sitinapulumuke.”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 8:20
7 Mawu Ofanana  

Wokolola m'malimwe ndi mwana wanzeru; koma wogona pakututa ndi mwana wochititsa manyazi.


Taonani, mau a kulira kwa mwana wamkazi wa anthu anga ochokera kudziko lakutali: Kodi mu Ziyoni mulibe Yehova? Kodi mulibe mfumu yake? Chifukwa chanji andiputa Ine ndi mafano ao osema, ndi zachabe zachilendo?


Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira.


Pamene atauka mwini nyumba natseka pakhomo, ndipo inu mudzayamba kuima pabwalo, ndi kugogoda pachitseko, ndi kunena, Ambuye titsegulireni ife; ndipo Iye adzayankha nadzati ndi inu, Sindidziwa inu kumene muchokerako;


ndipo adzakupasula iwe, ndi ana ako mwa iwe; ndipo sadzasiya mwa iwe mwala wina pamwala unzake; popeza sunazindikire nyengo ya mayang'aniridwe ako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa