Yeremiya 8:19 - Buku Lopatulika19 Taonani, mau a kulira kwa mwana wamkazi wa anthu anga ochokera kudziko lakutali: Kodi mu Ziyoni mulibe Yehova? Kodi mulibe mfumu yake? Chifukwa chanji andiputa Ine ndi mafano ao osema, ndi zachabe zachilendo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Taonani, mau a kulira kwa mwana wamkazi wa anthu anga ochokera kudziko lakutali: Kodi m'Ziyoni mulibe Yehova? Kodi mulibe mfumu yake? Chifukwa chanji andiputa Ine ndi mafano ao osema, ndi zachabe zachilendo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Imvani kulira kwa anthu anga kuchokera ku dziko lakutali. Akuti, “Kodi Chauta sali ku Ziyoni? Kodi mfumu yake siili kumeneko?” Chauta ayankha kuti, “Chifukwa chiyani akundiputa ndi mafano ao, ndiponso ndi milungu yao yachilendo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Imvani kulira kwa anthu anga kuchokera ku dziko lakutali: akuti, “Kodi Yehova sali ku Ziyoni? Kodi mfumu yake sili kumeneko?” “Chifukwa chiyani akundiputa ndi mafano awo osema, ndi milungu yawo yachilendo?” Onani mutuwo |