Yeremiya 8:18 - Buku Lopatulika18 Ha, ndikadatonthoza mtima wanga kuletsa chisoni chake? Mtima wanga walefuka m'kati mwa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ha, ndikadatonthoza mtima wanga kuletsa chisoni chake? Mtima wanga walefuka m'kati mwa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kudandaula kwanga nkosalekeza. Mtima wanga walefukiratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndadzazidwa ndi chisoni kwambiri, mtima wanga walefukiratu. Onani mutuwo |