Yeremiya 8:15 - Buku Lopatulika15 Tinayang'anira mtendere, koma panalibe zabwino; ndi nthawi ya moyo, ndipo taona kuopsedwa! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Tinayang'anira mtendere, koma panalibe zabwino; ndi nthawi ya moyo, ndipo taona kuopsedwa! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tinkafuna mtendere, koma zinthu sizidatiyendere bwino. Tinkafuna kuchira, koma tidangopeza zoopsa zokhazokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Tinkayembekezera mtendere koma palibe chabwino chomwe chinachitika, tinkayembekezera kuchira koma tinakumana ndi zoopsa zokhazokha. Onani mutuwo |