Yeremiya 8:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo analipoletsa pang'ono bala la mwana wamkazi wa anthu anga, ndi kuti, Mtendere, mtendere; posakhala mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo analipoletsa pang'ono bala la mwana wamkazi wa anthu anga, ndi kuti, Mtendere, mtendere; posakhala mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Iwo amapoletsa mabala a anthu anga pamwamba pokha. Amangonena kuti, ‘Kuli mtendere, kuli mtendere,’ chonsecho kulibe konse mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iwo amapoletsa zilonda za anthu anga pamwamba chabe nʼkumati, ‘Mtendere, mtendere,’ pamene palibe mtendere. Onani mutuwo |